Hoseya 7:16 - Buku Lopatulika16 Abwerera, koma si kwa Wam'mwambayo; akunga uta wosakhulupirika; akalonga ao adzagwa ndi lupanga mwa chipongwe cha lilime lao; ichi ndicho adzawasekera m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Abwerera, koma si kwa Wam'mwambayo; akunga uta wosakhulupirika; akalonga ao adzagwa ndi lupanga mwa chipongwe cha lilime lao; ichi ndicho adzawasekera m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Amatembenukira kwa mulungu wachabechabe, osati kwa Mulungu wopambanazonse. Ali ngati uta wokhota. Atsogoleri ao adzaphedwa ndi lupanga chifukwa chakuti amandilankhulira zachipongwe. Motero a ku Ejipito adzaŵaseka kwambiri.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Iwo satembenukira kwa Wammwambamwamba; ali ngati uta woonongeka. Atsogoleri awo adzaphedwa ndi lupanga chifukwa cha mawu awo achipongwe. Motero iwo adzasekedwa mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |
Pakuti atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Monga mkwiyo wanga ndi ukali wanga wathiridwa kwa okhala mu Yerusalemu, momwemo ukali wanga udzathiridwa pa inu, pamene mudzalowa mu Ejipito; ndipo mudzakhala chitukwano, ndi chizizwitso, ndi chitemberero, ndi chitonzo; ndipo simudzaonananso malo ano.