Hoseya 7:15 - Buku Lopatulika15 Chinkana ndawalangiza ndi lulimbitsa manja ao, andilingiririra choipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Chinkana ndawalangiza ndi lulimbitsa manja ao, andilingiririra choipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ngakhale ndimaŵalera ndi kuŵalimbitsa, komabe amandichita zachiwembu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ine ndinawaphunzitsa ndikuwalimbitsa, koma amandikonzera chiwembu. Onani mutuwo |