Hoseya 7:8 - Buku Lopatulika8 Efuremu asokonezana nayo mitundu ya anthu; Efuremu ndiye kamtanda ka mkate kosatembenuzidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Efuremu asokonezana nayo mitundu ya anthu; Efuremu ndiye kamtanda ka mkate kosatembenuzidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta akuti, “Aefuremu ali ngati keke yopsa kumodzi, chifukwa amasakanizikana ndi anthu a mitundu ina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Efereimu wasakanikirana ndi mitundu ya anthu ena; Efereimu ndi buledi amene wapsa mbali imodzi. Onani mutuwo |