Hoseya 7:7 - Buku Lopatulika7 Onsewo atentha ngati ng'anjo, natha oweruza ao, agwa mafumu ao onse; palibe mmodzi mwa iwo wakuitana Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Onsewo atentha ngati ng'anjo, natha oweruza ao, agwa mafumu ao onse; palibe mmodzi mwa iwo wakuitana Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Onsewo amakhala juu ngati uvuni, ndipo amapha olamulira ao. Imodziimodzi mafumu ao onse agwa, koma palibe ndi mmodzi yemwe wondiitana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Onsewa ndi otentha ngati uvuni, amapha olamulira awo. Mafumu awo onse amagwa, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amandiyitana Ine. Onani mutuwo |