Hoseya 6:11 - Buku Lopatulika11 Akuikidwiratunso nyengo yakukolola, Yuda iwe, pamene ndikabwezanso undende wa anthu anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Akuikidwiratunso nyengo yakukolola, Yuda iwe, pamene ndikabwezanso undende wa anthu anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 “Inunso Ayuda mudzakolola chilango. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 “Kunenanso za iwe Yuda, udzakolola chilango. “Pamene ndiwabwezere anthu anga zinthu zabwino.” Onani mutuwo |