Hoseya 5:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo kudzikuza kwa Israele kudzamchitira umboni pamaso pake; chifukwa chake Israele ndi Efuremu adzakhumudwa m'mphulupulu mwao; Yudanso adzakhumudwa pamodzi nao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo kudzikuza kwa Israele kudzamchitira umboni pamaso pake; chifukwa chake Israele ndi Efuremu adzakhumudwa m'mphulupulu mwao; Yudanso adzakhumudwa pamodzi nao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Kudzikuza kwa Israele kwasanduka umboni womutsutsa. Zoonadi Efuremu adzagwa ndi machimo ake. Nayenso Yuda adzateronso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kudzikuza kwa Israeli kwakhala umboni womutsutsa; Aisraeli, ngakhale Aefereimu, anagwa mʼmachimo awo; Yudanso anagwa nawo pamodzi. Onani mutuwo |