Hoseya 5:4 - Buku Lopatulika4 Machitidwe ao sawalola kubwerera kwa Mulungu wao; pakuti mzimu wa uhule uli m'kati mwao, ndipo sadziwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Machitidwe ao sawalola kubwerera kwa Mulungu wao; pakuti mzimu wa uhule uli m'kati mwao, ndipo sadziwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ntchito zao zoipa zatseka njira yao yobwerera kwa Mulungu wao, pakuti mtima wa kusakhulupirika uli mwa iwo, ndipo salabadako za Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Ntchito zawo siziwalola kubwerera kwa Mulungu wawo. Mʼmitima mwawo muli mzimu wachiwerewere; Iwo sadziwa Yehova. Onani mutuwo |