Hoseya 5:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo opandukawo analowadi m'zovunda; koma Ine ndine wakuwadzudzula onsewo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo opandukawo analowadi m'zovunda; koma Ine ndine wakuwadzudzula onsewo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Opandukawo azama kwambiri m'machimo ao, Ine ndidzaŵalanga onsewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Owukira azama mʼmoyo wakupha, Ine ndidzawalanga onsewo. Onani mutuwo |