Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Hoseya 5:2 - Buku Lopatulika

2 Ndipo opandukawo analowadi m'zovunda; koma Ine ndine wakuwadzudzula onsewo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Ndipo opandukawo analowadi m'zovunda; koma Ine ndine wakuwadzudzula onsewo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Opandukawo azama kwambiri m'machimo ao, Ine ndidzaŵalanga onsewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Owukira azama mʼmoyo wakupha, Ine ndidzawalanga onsewo.

Onani mutuwo Koperani




Hoseya 5:2
18 Mawu Ofanana  

Nanga bwanji mukali chimenyedwere kuti inu mulikupandukirabe? Mutu wonse ulikudwala, ndi mtima wonse walefuka.


Tsoka kwa iwo amene afunitsa kubisira Yehova uphungu wao, ndi ntchito zao zili mumdima, ndipo amati ndani ationa ife? Ndani atidziwa ife?


Ndipo iwo anati, Tiyeni, tilingalire Yeremiya chomchitira choipa; pakuti chilamulo sichidzathera wansembe, kapena uphungu wanzeru, kapena mau mneneri. Tiyeni, timpande iye ndi lilime, tisamvere iye mau ake ali onse.


Yehova Inu, maso anu sali pachoonadi kodi? Munawapanda iwo, koma sanaphwetekedwe mtima; munawatha iwo, koma akana kudzudzulidwa; alimbitsa nkhope zao koposa mwala; akana kubwera.


Onse ali opikisana ndithu, ayendayenda ndi maugogodi; ndiwo mkuwa ndi chitsulo; onsewa achita movunda;


Koma kulumbira, ndi kunama, ndi kupha, ndi kuba, ndi kuchita chigololo; aboola, ndi mwazi ukhudzana nao mwazi.


Chifukwa chake ndawalikha mwa aneneri; ndawapha ndi mau a pakamwa panga; ndi maweruzo anga atuluka ngati kuunika.


Ndipo monga magulu a mbala alalira munthu, momwemo msonkhano wa ansembe amapha panjira ya ku Sekemu; indedi achita choipitsitsa.


Choipa chao chonse chili mu Giligala; pakuti pamenepo ndinawada, chifukwa cha kuipa kwa machitidwe ao ndidzawainga kuwachotsa m'nyumba mwanga; sindidzawakondanso; akalonga ao onse ndiwo opanduka.


Onse amene ndiwakonda, ndiwadzudzula ndi kuwalanga; potero chita changu, nutembenuke mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa