Hoseya 5:1 - Buku Lopatulika1 Imvani ichi, ansembe inu; mverani, inu nyumba ya Israele; tcherani khutu, inu nyumba ya mfumu; pakuti chiweruzochi chinena inu; pakuti munakhala msampha ku Mizipa, ndi ukonde woyalidwa pa Tabori. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Imvani ichi, ansembe inu; mverani, inu nyumba ya Israele; tcherani khutu, inu nyumba ya mfumu; pakuti chiweruzochi chinena inu; pakuti munakhala msampha ku Mizipa, ndi ukonde woyalidwa pa Tabori. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Ansembe inu, imvani izi! Aisraele inu, mumvetsere nonse. Inu a m'banja la mfumu, mvetserani mau anga. Chilango chidzakugwerani, chifukwa inu munali msampha ku Mizipa, mudachita ngati kuyala ukonde ku phiri la Tabori. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Ansembe inu, imvani izi! Inu Aisraeli, tcherani khutu! Inu nyumba yaufumu, mvetserani! Chiweruzo ichi ndi chotsutsa inu: Inu munali ngati msampha ku Mizipa, munali ngati ukonde woyalidwa pa phiri la Tabori. Onani mutuwo |