Hoseya 4:19 - Buku Lopatulika19 Mphepo yamkulunga m'mapiko ake, ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Mphepo yamkulunga m'mapiko ake, ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Adzachotsedwa ngati chinthu chotengedwa ndi mphepo, ndipo adzachititsidwa manyazi chifukwa cha nsembe zao zachikunja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Adzachotsedwa ndi kamvuluvulu ndipo adzachita manyazi chifukwa cha nsembe zawo. Onani mutuwo |