Hoseya 4:8 - Buku Lopatulika8 Adyerera tchimo la anthu anga, nakhumbira chosalungama chao, yense ndi mtima wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Adyerera tchimo la anthu anga, nakhumbira chosalungama chao, yense ndi mtima wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Amalemererapo pa kuchimwa kwa anthu anga, ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azichimwirachimwira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Amalemererapo pa machimo a anthu anga ndipo amafunitsitsa kuti anthuwo azipitiriza kuchimwa. Onani mutuwo |