Hoseya 4:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kudzakhala monga anthu, momwemo wansembe; ndipo ndidzawalanga chifukwa chanjira zao, ndi kuwabwezera machitidwe ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kudzakhala monga anthu, momwemo wansembe; ndipo ndidzawalanga chifukwa chanjira zao, ndi kuwabwezera machitidwe ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tsono ansembewo ndidzaŵachita zomwe ndidzaŵachite anthu. Ndidzaŵalanga chifukwa cha makhalidwe ao oipa ndi kuŵalipsira pa ntchito zaozo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo zidzakhala motere: zochitikira anthu ena, zidzachitikiranso ansembe. Ndidzawalanga onsewo chifukwa cha njira zawo, ndidzawabwezera chifukwa cha machitidwe awo. Onani mutuwo |
Ndipo padzakhala monga ndi anthu, moteronso ndi ansembe; monga ndi mtumiki, moteronso ndi mbuyake; monga ndi mdzakazi, moteronso ndi mbuyake wamkazi; monga ndi wogula, moteronso ndi wogulitsa; monga ndi wobwereka, moteronso ndi wombwereka; monga ndi wotenga phindu, moteronso ndi wombwezera phindu kwa iye.