Hoseya 4:7 - Buku Lopatulika7 Monga anachuluka, momwemo anandichimwira; ndidzasanduliza ulemerero wao ukhale manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Monga anachuluka, momwemo anandichimwira; ndidzasanduliza ulemerero wao ukhale manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Ansembe ankati akamachulukirachulukira, ndi m'menenso ankanyanyira kundichimwira. Ndidzasandutsa ulemu wao kuti ukhale manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ansembe ankati akachuluka iwo ankandichimwiranso kwambiri; iwo anasinthanitsa ulemerero wawo ndi chinthu china chonyansa. Onani mutuwo |