Hoseya 4:2 - Buku Lopatulika2 Koma kulumbira, ndi kunama, ndi kupha, ndi kuba, ndi kuchita chigololo; aboola, ndi mwazi ukhudzana nao mwazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma kulumbira, ndi kunama, ndi kupha, ndi kuba, ndi kuchita chigololo; aboola, ndi mwazi ukhudzana nao mwazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Akulumbira monama, kunena zabodza, kupha, kuba ndi kuchita chigololo. Machimo achita kunyanya, ndipo akungophanaphana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha. Kuba ndi kuchita chigololo; machimo achita kunyanya ndipo akungokhalira kuphana. Onani mutuwo |