Hoseya 4:1 - Buku Lopatulika1 Imvani mau a Yehova, inu ana a Israele; pakuti Yehova ali ndi mlandu ndi okhala m'dziko, popeza palibe choonadi, kapena chifundo, kapena kudziwa Mulungu m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Imvani mau a Yehova, inu ana a Israele; pakuti Yehova ali ndi mlandu ndi okhala m'dziko, popeza palibe choonadi, kapena chifundo, kapena kudziwa Mulungu m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Aisraele, imvani mau a Chauta, chifukwa Iye akukuimbani mlandu, inu anthu okhala m'dziko. Mlandu wake ndi wakuti, m'dziko mulibe kukhulupirika kapena kukoma mtima, ndipo Mulungu samulabadira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Aisraeli, imvani mawu a Yehova, chifukwa Yehova ali ndi mlandu ndi inu amene mumakhala mʼdzikoli: “Mʼdziko mwanu mulibe kukhulupirika, mulibe chikondi mulibe kulabadira za Mulungu. Onani mutuwo |