Hoseya 3:5 - Buku Lopatulika5 atatero ana a Israele adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wake masiku otsiriza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 atatero ana a Israele adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wake masiku otsiriza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pambuyo pake Aisraelewo adzabwerera ndi kufunafuna Chauta Mulungu wao ndi mdzukulu wa Davide mfumu yao. Nthaŵi imeneyo Aisraele adzagonja kwa Chauta ndipo adzalandira zabwino zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pambuyo pake Aisraeli adzabwerera ndi kufunafuna Yehova Mulungu wawo ndi Davide mfumu yawo. Adzabwera kwa Yehova akunjenjemera ndipo adzalandira madalitso mʼmasiku awo otsiriza. Onani mutuwo |