Hoseya 4:3 - Buku Lopatulika3 Chifukwa chake dziko lidzachita chisoni, ndi aliyense wokhalamo adzalefuka, pamodzi ndi nyama zakuthengo, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndi nsomba za m'nyanja zomwe zidzachotsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Chifukwa chake dziko lidzachita chisoni, ndi aliyense wokhalamo adzalefuka, pamodzi ndi nyama za kuthengo, ndi mbalame za m'mlengalenga; ndi nsomba za m'nyanja zomwe zidzachotsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Nchifukwa chake mudzagwa chilala m'dziko, ndipo onse okhalamo adzavutika pamodzi ndi nyama zakuthengo zomwe, ndi mbalame zamumlengalenga. Ngakhale nsomba zam'nyanja zidzafa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Chifukwa chake dziko likulira ndipo onse amene amakhalamo akuvutika; zirombo zakuthengo ndi mbalame zamumlengalenga ndiponso nsomba zamʼnyanja zikufa. Onani mutuwo |