Hoseya 4:16 - Buku Lopatulika16 Pakuti Israele wachita kuuma khosi ngati ng'ombe yaikazi yaing'ono youma khosi; tsopano Yehova adzawadyetsa ngati mwanawankhosa kuthengo lalikulu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Pakuti Israele wachita kuuma khosi ngati ng'ombe yaikazi yaing'ono youma khosi; tsopano Yehova adzawadyetsa ngati mwanawankhosa kuthengo lalikulu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Aisraele ndi okanika ngati anaang'ombe. Kodi Chauta angathe kuŵadyetsa tsopano ngati anaankhosa pa busa lokoma? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Aisraeli ndi nkhutukumve, ngosamva ngati ana angʼombe. Kodi Yehova angathe kuwaweta bwanji ngati ana ankhosa pa msipu wabwino? Onani mutuwo |