Hoseya 4:17 - Buku Lopatulika17 Efuremu waphatikana ndi mafano, mlekeni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Efuremu waphatikana ndi mafano, mlekeni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Anthu a ku Efuremu aphathana ndi mafano, izo nzao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Efereimu waphathana ndi mafano; mulekeni! Onani mutuwo |