Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Hoseya 4:17 - Buku Lopatulika

17 Efuremu waphatikana ndi mafano, mlekeni.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Efuremu waphatikana ndi mafano, mlekeni.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 “Anthu a ku Efuremu aphathana ndi mafano, izo nzao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Efereimu waphathana ndi mafano; mulekeni!

Onani mutuwo Koperani




Hoseya 4:17
8 Mawu Ofanana  

Potero ndinawaperekera kuuma mtima kwao, ayende monga mwa uphungu waowao.


Monga anawaitana, momwemo anawachokera; anaphera nsembe Abaala, nafukizira mafano osema.


Ndi lupanga lidzagwera mizinda yake, lidzatha mipiringidzo yake, ndi kuononga chifukwa cha uphungu wao.


Efuremu akudya mphepo, natsata mphepo ya kum'mawa; tsiku lonse achulukitsa mabodza ndi chipasuko, ndipo achita pangano ndi Asiriya, natenga mafuta kunka nao ku Ejipito.


Ndipo tsopano aonjeza kuchimwa, nadzipangira mafano oyenga a siliva wao, mafano monga mwa nzeru zao, onsewo ntchito ya amisiri; anena za iwo, Anthu ophera nsembe apsompsone anaang'ombe.


Koma munthu asatsutsane ndi mnzake, kapena kudzudzula mnzake; popeza anthu ako ndiwo akunga otsutsana ndi wansembe.


Kawalekeni iwo, ali atsogoleri akhungu. Ndipo ngati wakhungu amtsogolera wakhungu, onse awiri adzagwa m'mbuna.


Iye wakukhala wosalungama achitebe zosalungama; ndi munthu wonyansa akhalebe wonyansa; ndi iye wakukhala wolungama achitebe cholungama; ndi iye amene ali woyera akhalebe woyeretsedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa