Hoseya 4:15 - Buku Lopatulika15 Chinkana iwe, Israele, uchita uhule, koma asapalamule Yuda; ndipo musafika inu ku Giligala, kapena kukwera ku Betaveni, kapena kulumbira, Pali Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Chinkana iwe, Israele, uchita uhule, koma asapalamule Yuda; ndipo musafika inu ku Giligala, kapena kukwera ku Betaveni, kapena kulumbira, Pali Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Ngakhale Aisraele amachita zosakhulupirika, anthu a ku Yuda asapezeke ndi mlandu wotere. Asapite kukapembedza ku Giligala kapena ku Betehaveni. Asakalumbirenso kumeneko kuti, ‘Pali Chauta wamoyo!’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Ngakhale umachita chigololo, iwe Israeli, Yuda asapezeke ndi mlandu wotere. “Usapite ku Giligala. Usapite ku Beti-Aveni. Ndipo usalumbire kuti, ‘Pali Yehova wamoyo!’ Onani mutuwo |