Hoseya 2:9 - Buku Lopatulika9 Chifukwa chake ndidzabwera ndi kuchotsa tirigu wanga m'nyengo yake, ndi vinyo wanga m'nthawi yake yoikika, ndi kukwatula ubweya wanga ndi thonje langa, zimene zikadafunda umaliseche wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Chifukwa chake ndidzabwera ndi kuchotsa tirigu wanga m'nyengo yake, ndi vinyo wanga m'nthawi yake yoikika, ndi kukwatula ubweya wanga ndi thonje langa, zimene zikadafunda umaliseche wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nchifukwa chake ndidzamlanda tirigu wanga pa nthaŵi yodula ndi vinyo wanga pa nthaŵi yofinya. Ndidzamlandanso ubweya ndi thonje langa zimene ankavalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Choncho Ine ndidzamulanda tirigu wanga pa nthawi yokolola, ndi vinyo wanga watsopano pa nthawi yopsinya mphesa. Ndidzamulanda ubweya ndi thonje langa, zomwe akanaphimba nazo umaliseche wake. Onani mutuwo |