Hoseya 2:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo tsopano ndidzaonetsa manyazi ake pamaso pa omkonda, popandanso wakumlanditsa m'dzanja langa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo tsopano ndidzaonetsa manyazi ake pamaso pa omkonda, popandanso wakumlanditsa m'dzanja langa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Motero ndidzaonetsa dama lake poyera kwa zibwenzi zake, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene adzampulumutse m'manja mwanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Motero tsopano ndidzaonetsa maliseche ake pamaso pa zibwenzi zake; palibe ndi mmodzi yemwe adzamupulumutse mʼmanja mwanga. Onani mutuwo |