Hoseya 2:14 - Buku Lopatulika14 Chifukwa chake taonani, ndidzamkopa ndi kunka naye kuchipululu, ndi kulankhula naye momkonda mtima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Chifukwa chake taonani, ndidzamkopa ndi kunka naye kuchipululu, ndi kulankhula naye momkonda mtima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Tsono tamverani, ndidzamkopa mkaziyo, ndidzapita naye ku chipululu ndi kukamsangalatsa ndi mau achikondi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Koma tsopano ndidzamukopa mkaziyo; ndidzapita naye ku chipululu ndipo ndidzamuyankhula mwachikondi. Onani mutuwo |