Hoseya 2:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ndidzampatsa minda yake yampesa kuyambira pomwepo, ndi chigwa cha Akori chikhale khomo la chiyembekezo; ndipo adzavomereza pomwepo monga masiku a ubwana wake, ndi monga tsiku lokwera iye kutuluka m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ndidzampatsa minda yake yamphesa kuyambira pomwepo, ndi chigwa cha Akori chikhale khomo la chiyembekezo; ndipo adzavomereza pomwepo monga masiku a ubwana wake, ndi monga tsiku lokwera iye kutuluka m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Kumeneko ndidzambwezera minda yake yamphesa. Ndidzasandutsa Chigwa cha Mavuto kuti chikhale chipata cha kuchiyembekezo. Ndipo kumeneko azidzandiyankha monga m'mene ankandiyankhira pa ubwana wake, atatuluka ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kumeneko ndidzamubwezera minda yake ya mpesa, ndipo ndidzasandutsa Chigwa cha Akori kukhala khomo la chiyembekezo. Kumeneko iye adzayimba nyimbo monga mʼmasiku a ubwana wake, monga tsiku limene anatuluka ku Igupto. Onani mutuwo |