Hoseya 2:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo ndidzamlanga chifukwa cha masiku a Abaala amene anawafukizira, navala mphete za m'mphuno, ndi zokometsera zake, natsata omkonda, nandiiwala Ine, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo ndidzamlanga chifukwa cha masiku a Abaala amene anawafukizira, navala mphete za m'mphuno, ndi zokometsera zake, natsata omkonda, nandiiwala Ine, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndidzamlanga chifukwa choti adafukiza lubani kwa Abaala pa zikondwerero zao. Ankadzikongoletsa povala mphete ndi mikanda yamtengowapatali, kuti azithamangira zibwenzi zake, Ine nkumandiiŵala. Ndatero Ine Chauta.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndidzamulanga chifukwa cha masiku amene anafukiza lubani kwa Abaala; anadzikongoletsa povala mphete ndi mikanda yamtengowapatali ndipo anathamangira zibwenzi zake, koma Ine anandiyiwala,” akutero Yehova. Onani mutuwo |