Hoseya 13:12 - Buku Lopatulika12 Mphulupulu ya Efuremu yamangika, tchimo lake lisungika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Mphulupulu ya Efuremu yamangika, tchimo lake lisungika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 “Kuipa kwa anthu a ku Efuremu kwalembedwa m'buku, buku lake la machimo ao ndalisunga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kulakwa kwa Efereimu kwasungidwa, machimo ake alembedwa mʼbuku. Onani mutuwo |