Hoseya 13:11 - Buku Lopatulika11 Ndinakupatsa mfumu mu mkwiyo wanga; ndinamchotsanso mu ukali wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndinakupatsa mfumu mu mkwiyo wanga; ndinamchotsanso m'ukali wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndidakupatsani mafumu mwachipsera mtima. Kenaka atandikwiyitsa, ndidaŵachotsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Choncho Ine ndinakupatsani mfumu mwachipseramtima, ndipo ndinayichotsa mwaukali. Onani mutuwo |