Hoseya 13:10 - Buku Lopatulika10 Ili kuti mfumu yako tsopano, kuti ikupulumutse m'mizinda yako yonse? Ndi oweruza ako amene unanena za iwo, Ndipatseni mfumu ndi akalonga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ili kuti mfumu yako tsopano, kuti ikupulumutse m'midzi yako yonse? Ndi oweruza ako amene unanena za iwo, Ndipatseni mfumu ndi akalonga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Inu munkati, ‘Tipatseni mfumu ndi atsogoleri.’ Nanga tsopano mfumu yanuyo, yoti ikulanditseni, ili kuti? Nanga atsogoleri anuwo, oti akutchinjirizeni, ali kuti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kodi mfumu yako ili kuti, kuti ikupulumutse? Olamulira ako a mʼmizinda yonse ali kuti, amene iwe unanena za iwo kuti, ‘Patseni mfumu ndi akalonga?’ Onani mutuwo |