Hoseya 13:13 - Buku Lopatulika13 Zowawa zonga za mkazi wobala zidzamgwera, ndiye mwana wopanda nzeru; pakuti pali nyengo yakuti asachedwe mobalira ana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Zowawa zonga za mkazi wobala zidzamgwera, ndiye mwana wopanda nzeru; pakuti pali nyengo yakuti asachedwe mobalira ana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Zoŵaŵa zonga za mkazi pobala mwana zidzaŵagwera. Akadapulumutsidwa, koma ali ngati mwana wopanda nzeru, wosafuna kutuluka pa nthaŵi yake yobadwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Zowawa zonga za mayi pa nthawi yobala mwana zamugwera, koma iye ndi mwana wopanda nzeru, pamene nthawi yake yobadwa yafika iyeyo safuna kutuluka mʼmimba mwa amayi ake. Onani mutuwo |