Hoseya 12:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yakobo anathawira kuthengo la Aramu, ndi Israele anagwira ntchito chifukwa cha mkazi, ndi chifukwa cha mkazi anaweta nkhosa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yakobo anathawira kuthengo la Aramu, ndi Israele anagwira ntchito chifukwa cha mkazi, ndi chifukwa cha mkazi anaweta nkhosa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 (Yakobe adathaŵira ku dziko la Aramu. Israeleyo adagwira ntchito kumeneko kuti apeze mkazi. Ankaŵeta nkhosa kuti akwatire mkaziyo). Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yakobo anathawira ku dziko la Aramu, Israeli anagwira ntchito kuti apeze mkazi, ndipo anaweta nkhosa kuti akwatire mkaziyo. Onani mutuwo |