Hoseya 12:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo mwa mneneri Yehova anakweretsa Israele kuchokera mu Ejipito, ndi mwa mneneri anasungika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo mwa mneneri Yehova anakweretsa Israele kuchokera m'Ejipito, ndi mwa mneneri anasungika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Chauta adatulutsa Aisraele ku Ejipito kudzera mwa mneneri. Ndipo mwa mneneriyo adaŵasungabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Yehova anagwiritsa ntchito mneneri kuti atulutse Israeli mu Igupto; kudzera mwa mneneriyo Iye anawasamalira. Onani mutuwo |