Hoseya 11:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anthu anga alimbika kubwerera m'mbuyo kundileka Ine; chinkana akawaitana atsate Iye ali m'mwamba, sadzakweza ndi mmodzi yense. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anthu anga alimbika kubwerera m'mbuyo kundileka Ine; chinkana akawaitana atsate Iye ali m'mwamba, sadzakweza ndi mmodzi yense. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Anthu anga akangamira zondipandukira Ine. Tsono adzalira chifukwa cha goli lachilango limene lili pa iwo, koma palibe amene adzaŵachotsere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Anthu anga atsimikiza zondifulatira Ine. Ngakhale atayitana Wammwambamwamba, sizidzatheka kuti Iye awakwezenso. Onani mutuwo |