Hoseya 11:6 - Buku Lopatulika6 Ndi lupanga lidzagwera mizinda yake, lidzatha mipiringidzo yake, ndi kuononga chifukwa cha uphungu wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndi lupanga lidzagwera midzi yake, lidzatha mipiringidzo yake, ndi kuononga chifukwa cha uphungu wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Nkhondo idzaononga mizinda yao. Adani adzaphwanya zipata za malinga ao ndi kuŵaononga, chifukwa chotsata nzeru zaokha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Malupanga adzangʼanima mʼmizinda yawo, ndipo adzawononga mipiringidzo ya zipata zawo nadzathetseratu malingaliro awo. Onani mutuwo |