Hoseya 11:5 - Buku Lopatulika5 Iye sadzabwerera kunka kudziko la Ejipito, koma Asiriya adzakhala mfumu yake, popeza anakana kubwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Iye sadzabwerera kunka kudziko la Ejipito, koma Asiriya adzakhala mfumu yake, popeza anakana kubwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Tsono anthuwo adzabwereranso ku ukapolo ku Ejipito. Aasiriya adzakhala oŵalamulira, pakuti iwo akana kubwerera kwa Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Sadzabwerera ku Igupto, koma Asiriya ndiye adzakhala mfumu yawo pakuti akana kutembenuka. Onani mutuwo |