Hoseya 11:2 - Buku Lopatulika2 Monga anawaitana, momwemo anawachokera; anaphera nsembe Abaala, nafukizira mafano osema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Monga anawaitana, momwemo anawachokera; anaphera nsembe Abaala, nafukizira mafano osema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ine ndikamakangaza kumuitana, iye ndiye kumandithaŵa kunka kutali. Ankaperekabe nsembe kwa Baala ndi kulitenthera lubani fanolo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Koma ndimati ndikamapitiriza kuyitana iwo amandithawa kupita kutali. Ankapereka nsembe kwa Abaala ndipo ankafukiza lubani kwa mafano. Onani mutuwo |