Hoseya 11:1 - Buku Lopatulika1 Pamene Israele anali mwana, ndinamkonda, ndinaitana mwana wanga ali mu Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamene Israele anali mwana, ndinamkonda, ndinaitana mwana wanga ali m'Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta akuti, “Pamene Israele anali mwana, ndinkamukonda. Mwana wangayo ndidamuitana kuti atuluke ku Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Israeli ali mwana, ndinamukonda, ndipo ndinayitana mwana wanga kuti atuluke mu Igupto. Onani mutuwo |