Hoseya 10:15 - Buku Lopatulika15 Momwemo adzakuchitirani Betele, chifukwa cha choipa chanu chachikulu; mbandakucha mfumu ya Israele idzalikhika konse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Momwemo adzakuchitirani Betele, chifukwa cha choipa chanu chachikulu; mbandakucha mfumu ya Israele idzalikhika konse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Momwemo zidzakuchitikirani inu a ku Betele chifukwa cha uchimo wanu waukulu. Nkhondo ikadzangoyamba m'mamaŵa, nayonso mfumu ya ku Israele idzaphedwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Momwemonso zidzakuchitikira, iwe Beteli chifukwa kuyipa kwako ndi kwakukulu. Tsiku limeneli likadzafika, mfumu ya Israeli idzawonongedwa kwathunthu. Onani mutuwo |