Hoseya 11:3 - Buku Lopatulika3 Koma Ine ndinaphunzitsa Efuremu kuyenda, ndinawafungata m'manja mwanga; koma sanadziwe kuti ndinawachiritsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Koma Ine ndinaphunzitsa Efuremu kuyenda, ndinawafungata m'manja mwanga; koma sanadziwe kuti ndinawachiritsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Komabe ndine amene ndidaphunzitsa Aefuremu kuyenda. Ndidaŵalera, koma sadavomereze kuti amene ndidaŵasamala ndine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ndi Ine amene ndinaphunzitsa Efereimu kuyenda, ndipo ndinawagwira pa mkono; koma iwo sanazindikire kuti ndine amene ndinawachiritsa. Onani mutuwo |