Hoseya 10:6 - Buku Lopatulika6 Adzachitengeranso ku Asiriya chikhale mphatso ya kwa mfumu Yarebu; Efuremu adzatenga manyazi, ndi Israele adzachita manyazi ndi uphungu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Adzachitengeranso ku Asiriya chikhale mphatso ya kwa mfumu Yarebu; Efuremu adzatenga manyazi, ndi Israele adzachita manyazi ndi uphungu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Zoonadi, fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya, kuti likakhale mphatso yoperekedwa kwa mfumu yaikulu. Aefuremu adzachita manyazi, Aisraelewo adzachita manyazi chifukwa cha malangizo onama amene ankamvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Fanolo lidzatengedwa kupita ku Asiriya ngati mphatso kwa mfumu yayikulu. Efereimu adzachititsidwa manyazi chifukwa cha mafano ake amitengo. Onani mutuwo |