Hoseya 10:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo Samariya, mfumu yake yamwelera ngati thovu pamadzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo Samariya, mfumu yake yamwelera ngati thovu pamadzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mfumu ya ku Samariya idzatengedwa kunka kutali ngati kanthambi koyenda pa madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Samariya ndi mfumu yake adzatengedwa kupita kutali ngati kanthambi koyenda pa madzi. Onani mutuwo |