Hoseya 10:4 - Buku Lopatulika4 Anena mau akulumbira monama, pakuchita mapangano momwemo; chiweruzo chiphuka ngati zitsamba zowawa m'michera ya munda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Anena mau akulumbira monama, pakuchita mapangano momwemo; chiweruzo chiphuka ngati zitsamba zowawa m'michera ya munda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mafumu akungolankhula mau opandapake. Amangochita zipangano ndi malonjezo abodza. Chilungamo chasanduka kusalungama kumene kumaphuka ngati udzu woipa m'munda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mafumu amalonjeza zambiri, amalumbira zabodza pochita mapangano. Kotero maweruzo amaphuka ngati zitsamba zakupha mʼmunda umene walimidwa. Onani mutuwo |