Hoseya 10:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti tsopano adzati, Tilibe mfumu, popeza sitiopa Yehova; ndi mfumu idzatichitira chiyani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti tsopano adzati, Tilibe mfumu, popeza sitiopa Yehova; ndi mfumu idzatichitira chiyani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Posachedwa anthuwo adzanena kuti, “Tilibe mfumu tsopano chifukwa sitidamvere Chauta. Komabe mfumuyo ikadatichitira chiyani ife?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamenepo anthuwo adzanena kuti, “Ife tilibe mfumu chifukwa sitinaope Yehova. Koma ngakhale tikanakhala ndi mfumu, kodi mfumuyo ikanatichitira chiyani?” Onani mutuwo |