Hoseya 10:10 - Buku Lopatulika10 Pamene ndifuna ndidzawalanga, ndi mitundu ya anthu idzawasonkhanira pomangidwa iwo pa zolakwa zao ziwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pamene ndifuna ndidzawalanga, ndi mitundu ya anthu idzawasonkhanira pomangidwa iwo pa zolakwa zao ziwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndidzabwera kudzalimbana ndi anthu aupanduŵa kuti ndiŵalange. Anthu a mitundu ina adzasonkhana kuti aŵathire nkhondo chifukwa cha uchimo wao waukulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pamene ndifunire, ndidzalanga anthuwo; mitundu ya anthu idzasonkhanitsidwa kudzalimbana nawo, kuwayika mʼndende chifukwa cha uchimo wawo waukulu. Onani mutuwo |