Hoseya 10:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Efuremu ndiye ng'ombe yaikazi yaing'ono, yozereweredwa, yokonda kupuntha tirigu; koma ndapita pa khosi lake lokoma; ndidzamsenzetsa Efuremu goli; Yuda adzalima, Yakobo adzaphwanya chibuluma chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Efuremu ndiye ng'ombe yaikazi yaing'ono, yozereweredwa, yokonda kupuntha tirigu; koma ndapita pa khosi lake lokoma; ndidzamsenzetsa Efuremu goli; Yuda adzalima, Yakobo adzaphwanya chibuluma chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kale Efuremu anali ngati ng'ombe yophunzitsidwa imene inkakonda kupuntha tirigu. Tsopano m'khosi lake lokongola ndaikamo goli, kuti agwire ntchito koposa. Ndifuna kuti Yuda azitipula, Yakobe azimwanya mauma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Efereimu ndi mwana wangʼombe wamkazi wophunzitsidwa amene amakonda kupuntha tirigu, choncho Ine ndidzayika goli mʼkhosi lake lokongolalo. Ndidzasenzetsa Efereimu goli, Yuda ayenera kulima, ndipo Yakobo ayenera kutipula. Onani mutuwo |