Hagai 1:2 - Buku Lopatulika2 Atero Yehova wa makamu, akuti, Anthu awa anena, Nthawi siinafike, nthawi yakumanga nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Atero Yehova wa makamu, akuti, Anthu awa anena, Nthawi siinafike, nthawi yakumanga nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Zimene ndikunena Ine Chauta Wamphamvuzonse ndi izi: Anthu aŵa amanena kuti, ‘Nthaŵi siinafike yoti nkumanganso Nyumba ya Chauta.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu awa amanena kuti, ‘Nthawi sinafike yoti nʼkumanga Nyumba ya Yehova.’ ” Onani mutuwo |