Genesis 9:27 - Buku Lopatulika27 Mulungu akuze Yafeti, akhale iye m'mahema a Semu; Kanani akhale kapolo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Mulungu akuze Yafeti, akhale iye m'mahema a Semu; Kanani akhale kapolo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Mulungu amkuze Yafeti. Zidzukulu zake zidzagaŵane madalitso ndi zidzukulu za Semu. Kanani adzakhale kapolo wa Yafetiyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Mulungu akulitse dziko la Yafeti; Yafeti alandire madalitso pamodzi ndi Semu, ndipo Kanaani akhale kapolo wawo.” Onani mutuwo |
Ndipo ndidzaika chizindikiro pakati pao, ndipo ndidzatumiza onse amene apulumuka mwa iwo kwa amitundu, kwa Tarisisi, kwa Puti ndi kwa Aludi, okoka uta kwa Tubala ndi Yavani, kuzisumbu zakutali, amene sanamve mbiri yanga, ngakhale kuona ulemerero wanga; ndipo adzabukitsa ulemerero wanga pakati pa amitundu.