Genesis 7:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu padziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo madzi anapambana, nachuluka ndithu pa dziko lapansi, ndipo chingalawa chinayandama pamadzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Madziwo adanka nakwererakwerera, ndipo chombocho chidayandama pa madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Madzi anafika mwamphamvu ndipo anachulukirachulukira pa dziko lapansi moti chombo chinayandama pamwamba pa madziwo. Onani mutuwo |