Genesis 6:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Yehova anamva chisoni chifukwa anapanga munthu padziko lapansi, ndipo anavutika m'mtima mwake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Yehova anamva chisoni chifukwa anapanga munthu pa dziko lapansi, ndipo anavutika m'mtima mwake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 adamva chisoni kuti adalenga anthu ndi kuŵakhazika pa dziko lapansi, ndipo adavutika mu mtima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova anamva chisoni kuti analenga munthu ndi kumuyika pa dziko lapansi, ndipo anawawidwa mtima. Onani mutuwo |