Genesis 6:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo panali pamene anthu anayamba kuchuluka padziko, ndi ana aakazi anawabadwira iwo, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo panali pamene anthu anayamba kuchuluka padziko, ndi ana akazi anawabadwira iwo, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nthaŵi imeneyo anthu anali atayamba kuchuluka pa dziko lonse lapansi, ndipo adabereka ana aakazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Anthu atayamba kuchuluka pa dziko lapansi ndi kubereka ana aakazi, Onani mutuwo |