Genesis 6:2 - Buku Lopatulika2 kuti ana aamuna a Mulungu anayang'ana ana aakazi a anthu, kuti iwo anali okongola; ndipo anadzitengera okha akazi onse amene anawasankha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 kuti ana amuna a Mulungu anayang'ana ana akazi a anthu, kuti iwo anali okongola; ndipo anadzitengera okha akazi onse amene anawasankha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ana aamuna a Mulungu adaona kuti ana aakazi a anthu anali okongola, nayamba kukwatira amene ankaŵakonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 ana aamuna a Mulungu anaona kuti ana aakazi a anthuwo anali okongola. Ndipo anakwatira aliyense amene anamusankha. Onani mutuwo |